Home Politics Phungu wa dera la kum’mwera cha ku m’mawa kwa mzinda wa Blantyre Sameer Suleiman apambana pachisankho chachipulula atogonjeza a Wild Ndipo yemwe ndi mfumu yakale ya mzinda wa Blantyre

Phungu wa dera la kum’mwera cha ku m’mawa kwa mzinda wa Blantyre Sameer Suleiman apambana pachisankho chachipulula atogonjeza a Wild Ndipo yemwe ndi mfumu yakale ya mzinda wa Blantyre

by Kingsley Sowa
0 comments

Phungu wanyumba yamalamulo kudera la Kum’mwera- chakum’mawa Kwa mzinda wa Blantyre a Sameer Suleiman apambana pachisankho chachipululala chomwe chachitika kuderali lachiwiri.

A Suleiman apambana pachisankhochi ndi mavoti 458 pamene yemwe amapikisana nawo a Wild Ndipo apeza mavoti 17.

Izi zikutanthauza kuti a Suleiman ndi omwe adzaimire pampando waphungu wanyumba yamalamulo pachipani Cha DPP kudera la Chigumula-BCA -Club Banana pachisankhochi chapa 16 September Chaka chino.

You may also like

Leave a Comment

Dowa Community Radio is a community-based radio station established in 2020 to be used as a tool of communication in Dowa district and surrounding areas to facilitate issues of Education, gender-based violence, culture, child trafficking, Agriculture, Climate change and environment, transparency and accountability, sports, community self reliance, and many more.

Newsletter

@2025 – All Right Reserved. MACRA Community Radios

Are you sure want to unlock this post?
Unlock left : 0
Are you sure want to cancel subscription?
-
00:00
00:00
Update Required Flash plugin
-
00:00
00:00

Connection Information

To perform the requested action, WordPress needs to access your web server. Please enter your FTP credentials to proceed. If you do not remember your credentials, you should contact your web host.

Connection Type