Home Politics A Enala Yesaya achipani cha MCP apambana pazisankho zachipulula za aphungu kudera la Blantyre-Chichiri-Misesa.

A Enala Yesaya achipani cha MCP apambana pazisankho zachipulula za aphungu kudera la Blantyre-Chichiri-Misesa.

by Kingsley Sowa
0 comments

Yemwe akuimila paudindo waphungu kudera Blantyre-Chichiri-Misesa muchipani cha Malawi congress-MCP Enala Yesaya wapambana pachisankho chachipulula chomwe chachitika lachitatu pasukulu ya pulaimale ya Kanjedza.

A Yesaya apambana pachisankhochi ndi mavoti 287 kugonjetsa a Charles Mwambyale omwe apeza mavoti 45.

Iwo ati ndiwokondwa ndi kupambanaku ponena kuti kukutanthauza chikhulupiliro chomwe anthu akuderali alinacho pokweza amayi paudindo.

A Yesaya alimbikitsa anthu akuderali kuti apitilire kukhala pambuyo pawo mpaka patsiku lachisankho pomwe ati ndi wodzipereka kutukula derali.

Kumbali yake wachiwiri kwa mkulu wa achinyamata muchipani cha MCP a Isaac Ramsey Khan anati chisankhochi chayenda bwino ndipo ayamikila anthu otsatira chipanichi potsatira ndondomeko za demokalase posankha munthu wamkazi paudindowu.

You may also like

Leave a Comment

Dowa Community Radio is a community-based radio station established in 2020 to be used as a tool of communication in Dowa district and surrounding areas to facilitate issues of Education, gender-based violence, culture, child trafficking, Agriculture, Climate change and environment, transparency and accountability, sports, community self reliance, and many more.

Newsletter

@2025 – All Right Reserved. MACRA Community Radios

Are you sure want to unlock this post?
Unlock left : 0
Are you sure want to cancel subscription?
-
00:00
00:00
Update Required Flash plugin
-
00:00
00:00

Connection Information

To perform the requested action, WordPress needs to access your web server. Please enter your FTP credentials to proceed. If you do not remember your credentials, you should contact your web host.

Connection Type