Home Crime Polisi ya Limbe yatsimikiza za imfa ya bamboo wa zaka 66 Davison Tambala yemwe wazipha yekha kudera la mfumu Chipagala ku BCA mu mzinda wa Blantyre.

Polisi ya Limbe yatsimikiza za imfa ya bamboo wa zaka 66 Davison Tambala yemwe wazipha yekha kudera la mfumu Chipagala ku BCA mu mzinda wa Blantyre.

by Kingsley Sowa
0 comments

Malinga ndi wachiwiri kwa mneneri wa polisi ya Limbe Sub Inspector Sam Kadyole, thupi la bambo Tambala linapezedwa likulendewera kudenga la nyumba yawo madzulo a lachiwiri pa 17 June.

Sub Inspector Kadyole auza Eagle FM online kuti kafukufuku akadadali mkati pakadalipanno ofuna kupeza chomwe bamboyu wadziphera.

Iwo apempha mzika za dziko lino kumafunsila uphungu oyenera kunthambi ya Victim support unit yomwe imapezeka pa polisi iliyonse yomwe alinayo pafupi pamene akumana ndi mavuto osiyanasiyana m’malo mochotsa moyo wawo.

M’mawu ake mfumu Chipagala yati izi ndi zodandaulitsa kaamba koti akhala akulimbikitsa anthu awo kuti azitha kugawana ndi anzawo komanso atsogoleri amipingo zankhawa zomwe akukumana nazo pamoyo wawo wa tsiku ndi tsiku.

You may also like

Leave a Comment

Dowa Community Radio is a community-based radio station established in 2020 to be used as a tool of communication in Dowa district and surrounding areas to facilitate issues of Education, gender-based violence, culture, child trafficking, Agriculture, Climate change and environment, transparency and accountability, sports, community self reliance, and many more.

Newsletter

@2025 – All Right Reserved. MACRA Community Radios

Are you sure want to unlock this post?
Unlock left : 0
Are you sure want to cancel subscription?
-
00:00
00:00
Update Required Flash plugin
-
00:00
00:00

Connection Information

To perform the requested action, WordPress needs to access your web server. Please enter your FTP credentials to proceed. If you do not remember your credentials, you should contact your web host.

Connection Type