National

Mtsogoleri wachipani cha Malawi congress Dr. Lazarus Mccarthy Chakwera avomereza kugonja pachisankho chomwe chinachitika pa 16 September chaka chino. Dr. Chakwera avomereza…

Read more

Motorcycle operators have been reminded to register their bikes and obtain licenses before the end of the last phase of registration window…

Read more

Gulu la mzika zokhudzidwa la union of concerned citizens’ lalimbikitsa a Malawi kukhala a mtendere pamene tsiku loponya voti likuwandikila. Izi zayankhulidwa…

Read more

Ngati njira imodzi yoonetsetsa kuti atsogoleri amipingo maka akumadera akumidzi ali ndi chokudya chokwanira, bungwe la Chiyembekezo center for transformation lalimbikitsa ntchito yophunzitsa abusa komanso atsogoleri amipingo zamomwe angapangile feteleza pogwiritsa ntchito zipangizo zopezeka m’madera mwawo m’boma la Phalombe.

Lachiwiri pa 17 June, Bungweli laphunzitsa abusa komanso atsogoleri amipingo makumi awiri ochokera mipingo yosiyanasiyana omwe ali pansi pagulu la Leyman Pastors…

Read more