Home Crime Apolisi ku Limbe amanga bambo wazaka 24 kamba komanimiza anthu kuti ndi msilikali wa MDF

Apolisi ku Limbe amanga bambo wazaka 24 kamba komanimiza anthu kuti ndi msilikali wa MDF

by Kingsley Sowa
0 comments

Apolisi ku Limbe akusunga mchitolokosi cha apolisi bambo wazaka 24 Emmanuel Davie pomuganizira kuti amanamiza anthu kuti ndi msilikali wa Malawi Defense Force- MDF.

Malingana ndi wachiwiri kwa mneneri wa polisi ya Limbe Sub-inspector Chibisa Mulimbika, bamboo oganizilidwayu wakhala akubela ndalama kwa anthu ochokera kudera la Bangwe.

A Mulimbika awuza eagle online kuti oganizilidwayu amavala unifolomu yachisilikali ndipo anaonedwa kudera la Chipagala komwe amabela anthu ndalama powanamiza kuti awalemba ntchito kunthambi ya asilikali mtsogolo muno.

Sub Inspector Mulimbika anati anthuwa anakaneneza bamboo oganizilidwayu kupolisi ya Bangwe komwe apolisi ofufuza anakwanitsa kumanga mkuluyu kutsatira kafukufuku yemwe anachita kuphatikizirapo kunthambi ya Asilikali ya MDF komwe anatsikimiza kuti mbamboyu samagwira ntchito kunthambiyi.

Picture: Sub inspector Chibisa Mulimbika

You may also like

Leave a Comment

Dowa Community Radio is a community-based radio station established in 2020 to be used as a tool of communication in Dowa district and surrounding areas to facilitate issues of Education, gender-based violence, culture, child trafficking, Agriculture, Climate change and environment, transparency and accountability, sports, community self reliance, and many more.

Newsletter

@2025 – All Right Reserved. MACRA Community Radios

Are you sure want to unlock this post?
Unlock left : 0
Are you sure want to cancel subscription?
-
00:00
00:00
Update Required Flash plugin
-
00:00
00:00

Connection Information

To perform the requested action, WordPress needs to access your web server. Please enter your FTP credentials to proceed. If you do not remember your credentials, you should contact your web host.

Connection Type