Khansala wadera la Chigumula a Wild Ndipo omwe anagonja pachisankho chachipulula kwa a Sameer Suleiman pachipani cha Democratic progressive-DPP ati ayimila derali…
Khansala wadera la Chigumula a Wild Ndipo omwe anagonja pachisankho chachipulula kwa a Sameer Suleiman pachipani cha Democratic progressive-DPP ati ayimila derali…
Ngati njira imodzi yoonetsetsa kuti chitetezo ndi chokhwima kudera la Limbe, kampani ya Premier Bet lachisanu yapereka thandizo la ndalama zokwana 1…
Malinga ndi wachiwiri kwa mneneri wa polisi ya Limbe Sub Inspector Sam Kadyole, thupi la bambo Tambala linapezedwa likulendewera kudenga la nyumba…
Lachiwiri pa 17 June, Bungweli laphunzitsa abusa komanso atsogoleri amipingo makumi awiri ochokera mipingo yosiyanasiyana omwe ali pansi pagulu la Leyman Pastors…
Gulu la ophunzira omwe anaphunzira pasukulu ya sekondale ya Mulanje muzaka zapakati pa 2008 ndi 2011 lati likukonza zopeza njira zosiyanasiyana zopezera…
Yemwe akuimira pa mpando wa khansala woima payekha kudera la BCA-Chigumula mumzinda wa Blantyre a Sadana Bakili atsindika kufunika koti atsogoleri azitengapo…